Marko 9:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Iye anafunsa atate wake, kuti, Chimenechi chinayamba kumgwira liti? Ndipo anati, Chidamyamba akali mwana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Iye anafunsa atate wake, kuti, Chimenechi chinayamba kumgwira liti? Ndipo anati, Chidamyamba akali mwana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Yesu adafunsa bambo wake uja kuti, “Kodi zimenezi zidamuyamba liti?” Bambo wakeyo adati, “Zidamuyamba ali mwana ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Yesu anafunsa abambo a mnyamatayo kuti, “Kodi wakhala chotere nthawi yayitali bwanji?” Iye anayankha kuti, “Kuyambira ali wamngʼono, Onani mutuwo |