Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 9:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo anawafunsa iwo, Mufunsana nao chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo anawafunsa iwo, Mufunsana nao chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Iye adaŵafunsa kuti, “Kodi mukutsutsana zotani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Iye anafunsa kuti, “Mukukangana nawo chiyani iwowa?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:16
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi anatuluka, nayamba kufunsana naye, ndi kufuna kwa Iye chizindikiro chochokera Kumwamba, namuyesa Iye.


Ndipo pomwepo anthu onse a khamulo, pakumuona Iye, anazizwa kwambiri, namthamangira Iye, namlonjera.


Ndipo wina wa m'khamulo anamyankha Iye, kuti, Mphunzitsi, ndadza naye kwa Inu mwana wanga, ali nao mzimu wosalankhula;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa