Marko 9:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo pomwepo anthu onse a khamulo, pakumuona Iye, anazizwa kwambiri, namthamangira Iye, namlonjera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo pomwepo anthu onse a khamulo, pakumuona Iye, anazizwa kwambiri, namthamangira Iye, namlonjera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Pamene anthu onsewo adaona Yesu, adadabwa kwambiri, ndipo adamthamangira kudzamlonjera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Nthawi yomweyo anthu onse atamuona, anadabwa kwambiri ndipo anathamanga kukamulonjera. Onani mutuwo |