Marko 8:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo anawauzitsa iwo kuti asanene kwa munthu mmodzi za Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo anawauzitsa iwo kuti asanene kwa munthu mmodzi za Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Yesu adaŵalamula kuti asauze munthu wina aliyense za Iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Yesu anawachenjeza kuti asawuze wina aliyense za Iye. Onani mutuwo |