Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo anawauzitsa iwo kuti asanene kwa munthu mmodzi za Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo anawauzitsa iwo kuti asanene kwa munthu mmodzi za Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Yesu adaŵalamula kuti asauze munthu wina aliyense za Iye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Yesu anawachenjeza kuti asawuze wina aliyense za Iye.

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:30
6 Mawu Ofanana  

Pamenepo analamulira ophunzira kuti asauze munthu kuti Iye ndiye Khristu.


Ndipo Yesu ananena naye, Ona, iwe, usauze munthu; koma muka, udzionetse wekha kwa wansembe, nupereke mtulo umene anaulamulira Mose, ukhale mboni kwa iwo.


Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana.


Ndipo anamtumiza amuke kwao, nanena, Usalowe konse m'mudzi.


Ndipo pakutsika iwo paphiri, Iye anawalamula kuti asauze munthu zinthu zimene adaziona, koma pamene Mwana wa Munthu akadzauka kwa akufa.


Ndipo Iye anawauzitsa iwo, nalamulira kuti asanene ichi kwa munthu aliyense;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa