Marko 8:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Iye anawafunsa, Koma inu munena kuti ndine yani? Petro anayankha nanena naye, Ndinu Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Iye anawafunsa, Koma inu munena kuti ndine yani? Petro anayankha nanena naye, Ndinu Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Apo Yesu adaŵafunsa kuti, “Nanga inuyo, mumati ndine yani?” Petro adamuyankha kuti, “Inu ndinu Mpulumutsi wolonjezedwa uja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Iye anafunsa kuti, “Koma nanga inu, mumati ndine yani?” Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu.” Onani mutuwo |