Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo Iye ananena nao, Simudziwitsa ngakhale tsopano kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo Iye ananena nao, Simudziwitsa ngakhale tsopano kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Apo Yesu adati, “Nanga ndiye simunamvetsebe?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Iye anawafunsa kuti, “Kodi simumvetsetsabe?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:21
10 Mawu Ofanana  

Zindikirani, opulukira inu mwa anthu; ndipo opusa inu, mudzachita mwanzeru liti?


pakuti sanazindikire za mikateyo, koma mitima yao inauma.


Ndipo anausitsa moyo m'mzimu wake, nanena, Anthu a mbadwo uno afunafuna chizindikiro bwanji? Indetu ndinena kwa inu, ngati chizindikiro chidzapatsidwa kwa mbadwo uno!


Ndipo Yesu pamene anazindikira, ananena nao, Bwanji mutsutsana chifukwa mulibe mkate? Kodi kufikira tsopano simuzindikira, nisimudziwitsa? Kodi muli nayo mitima yanu youma?


Ndipo anadza ku Betsaida. Ndipo anadza naye kwa Iye munthu wakhungu, nampempha Iye kuti amkhudze.


Ndipo Iye anawayankha nanena, Mbadwo wosakhulupirira inu, ndidzakhala ndi inu kufikira liti? Ndidzakulekererani nthawi yanji? Mudze naye kwa Ine.


Yesu ananena naye, Kodi ndili ndi inu nthawi yaikulu yotere, ndipo sunandizindikire, Filipo? Iye amene wandiona Ine waona Atate; unena iwe bwanji, Mutionetsere Atate?


Ukani molungama, ndipo musachimwe; pakuti ena alibe chidziwitso cha Mulungu. Ndilankhula kunyaza inu.


Ndinena ichi kukuchititsani inu manyazi. Kodi nkutero kuti mwa inu palibe mmodzi wanzeru, amene adzakhoza kuweruza pa abale,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa