Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:1 - Buku Lopatulika

1 Masiku ajawo pakukhalanso khamu lalikulu la anthu, ndipo analibe kanthu kakudya, Iye anadziitanira ophunzira ake, nanena nao,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Masiku ajawo pakukhalanso khamu lalikulu la anthu, ndipo analibe kanthu kakudya, Iye anadziitanira ophunzira ake, nanena nao,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Pasanapite nthaŵi yaitali anthu ambirimbiri adasonkhananso. Pamene Yesu adaona kuti anthuwo alibe chakudya, adaitana ophunzira ake naŵauza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mʼmasiku amenewo gulu lina lalikulu la anthu linasonkhana. Popeza iwo analibe chakudya, Yesu anayitana ophunzira ake nati kwa iwo,

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:1
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anadabwa kwakukulukulu, nanena, Wachita Iye zonse bwino; angakhale ogontha awamvetsa, ndi osalankhula awalankhulitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa