Marko 7:34 - Buku Lopatulika34 nagadamira kumwamba, nausa moyo, nanena naye, Efata, ndiko, Tatseguka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 nagadamira kumwamba, nausa moyo, nanena naye, Efata, ndiko, Tatseguka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Adayang'ana kumwamba, nadzuma, nkumuuza kuti, “Efata!” ndiye kuti “Tsekuka!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Iye anayangʼana kumwamba ndipo ndi mawu otsitsa moyo, anati kwa iye, “Efataa!” (Kutanthauza kuti, “Tsekuka!”) Onani mutuwo |