Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 7:35 - Buku Lopatulika

35 Ndipo makutu ake anatseguka, ndi chomangira lilime lake chinamasulidwa, ndipo analankhula chilunjikire.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Ndipo makutu ake anatsegula, ndi chomangira lilime lake chinamasulidwa, ndipo analankhula chilunjikire.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Pomwepo makutu a munthuyo adatsekuka, ndipo chimene chinkamanga lilime lake chidamasuka, mpaka adayamba kulankhula bwino lomwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Atachita izi, makutu a munthuyo anatsekuka komanso lilime lake linamasuka ndipo anayamba kuyankhula momveka bwino.

Onani mutuwo Koperani




Marko 7:35
7 Mawu Ofanana  

Pakuti ananena, ndipo chinachitidwa; analamulira, ndipo chinakhazikika.


akhungu alandira kuona kwao, ndi opunduka miyendo ayenda, akhate akonzedwa, ndi ogontha akumva, ndi akufa aukitsidwa, ndi kwa aumphawi ulalikidwa Uthenga Wabwino.


Ndipo ananyamuka iye pomwepo, nasenza mphasa, natuluka pamaso pa iwo onse; kotero kuti anadabwa onse, nalemekeza Mulungu, nanena kuti, Zotere sitinazione ndi kale lonse.


nagadamira kumwamba, nausa moyo, nanena naye, Efata, ndiko, Tatseguka.


Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa