Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 7:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo anadza naye kwa Iye munthu wogontha, ndi wachibwibwi; ndipo anampempha Iye kuti aike dzanja pa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo anadza naye kwa Iye munthu wogontha, ndi wachibwibwi; ndipo anampempha Iye kuti aike dzanja pa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Anthu ena adabwera kwa Iye ndi munthu yemwe anali gonthi ndi wolankhula movutikira. Anthuwo adapempha Yesu kuti amchiritse pomusanjika manja munthuyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Kumeneko anthu ena anabweretsa kwa Iye munthu amene anali wosamva ndi wosayankhula, ndipo anamupempha kuti asanjike dzanja pa iye.

Onani mutuwo Koperani




Marko 7:32
4 Mawu Ofanana  

nanena, kuti, Kamwana kanga kabuthu kalinkutsirizika; ndikupemphani Inu mufikeko, muike manja anu pa iko, kuti kapulumuke, ndi kukhala ndi moyo.


Ndipo makutu ake anatseguka, ndi chomangira lilime lake chinamasulidwa, ndipo analankhula chilunjikire.


Ndipo analikutulutsa chiwanda chosalankhula. Ndipo kunali, chitatuluka chiwanda, wosalankhulayo analankhula; ndipo makamu a anthu anazizwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa