Marko 7:26 - Buku Lopatulika26 Koma mkaziyo anali Mgriki, mtundu wake Msiro-Fenisiya. Ndipo anampempha Iye kuti atulutse chiwanda m'mwana wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Koma mkaziyo anali Mgriki, mtundu wake Msiro-Fenisiya. Ndipo anampempha Iye kuti atulutse chiwanda m'mwana wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Maiyo anali mkunja, wa mtundu wa anthu a ku Siro-Fenisiya. Adapempha Yesu kuti akatulutse mzimu woipawo mwa mwana wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Mayiyu anali Mhelene, wobadwira ku Fonisia wa ku Siriya. Anamupempha Yesu kuti atulutse chiwanda mwa mwana wake. Onani mutuwo |