Marko 7:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo ananena naye, Baleka, ayambe akhuta ana; pakuti si kwabwino kuti titenge mkate wa ana, ndi kuutayira tiagalu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo ananena naye, Baleka, athange akhuta ana; pakuti si kwabwino kuti titenge mkate wa ana, ndi kuutayira tiagalu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma Yesu adamuyankha kuti, “Ai, alekeni ana ayambe adya nkukhuta. Sibwino kutenga chakudya cha ana nkuponyera agalu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Iye anamuwuza kuti, “Choyamba asiye ana adye zimene akuzifuna, pakuti si kwabwino kutenga buledi wa ana ndi kuponyera agalu awo.” Onani mutuwo |