Marko 7:23 - Buku Lopatulika23 zoipa izi zonse zituluka m'kati, nkudetsa munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 zoipa izi zonse zituluka m'kati, nizidetsa munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Zoipa zonsezi zimachokera m'kati mwa munthu, ndipo ndizo zimamuipitsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Zoyipa zonsezi zimatuluka mʼkati ndipo zimadetsa munthu.” Onani mutuwo |