Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 7:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo anati, Chotuluka mwa munthu ndicho chidetsa munthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo anati, Chotuluka mwa munthu ndicho chidetsa munthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Adatinso, “Zimene zimatuluka mwa munthu, ndizo zimamuipitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Anapitiriza kuti, “Chimene chichokera mwa munthu ndi chomwe chimamudetsa.

Onani mutuwo Koperani




Marko 7:20
12 Mawu Ofanana  

Ndipo akadza kundiona wina angonena bodza; mumtima mwake adzisonkhera zopanda pake, akanka nayenda namakanena.


Tsoka iwo akulingirira chinyengo, ndi kukonza choipa pakama pao! Kutacha m'mawa achichita, popeza chikhozeka m'manja mwao.


Koma zakutuluka m'kamwa zichokera mumtima; ndizo ziipitsa munthu.


Koma Iye anayankha nati, Kwalembedwa, Munthu sadzakhala ndi moyo ndi mkate wokha, koma ndi mau onse akutuluka m'kamwa mwa Mulungu.


kulibe kanthu kunja kwa munthu kukalowa mwa iye, kangathe kumdetsa: koma zinthu zakutuluka mwa munthu, ndizo zakumdetsa munthu.


Pakuti m'kati mwake mwa mitima ya anthu, mutuluka maganizo oipa, zachiwerewere,


zoipa izi zonse zituluka m'kati, nkudetsa munthu.


koma iye amene mawerengedwe a chibadwidwe chake sachokera mwa iwo, anatenga limodzi la magawo khumi kwa Abrahamu, namdalitsa iye amene ali nao malonjezano.


Ndipo lilime ndilo moto; ngati dziko la chosalungama mwa ziwalo zathu laikika lilime, ndili lodetsa thupi lonse, niliyatsa mayendedwe a chibadwidwe, ndipo liyatsidwa ndi Gehena.


Zichokera kuti nkhondo, zichokera kuti zolimbana mwa inu? Kodi sizichokera kuzikhumbitso zanu zochita nkhondo m'ziwalo zanu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa