Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 6:54 - Buku Lopatulika

54 Ndipo pamene anatuluka m'ngalawa anamzindikira pomwepo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Ndipo pamene anatuluka m'ngalawa anamzindikira pomwepo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Pamene iwo adatuluka m'chombomo, nthaŵi yomweyo anthu adamzindikira Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Atangotuluka mʼbwato, anthu anamuzindikira Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 6:54
5 Mawu Ofanana  

ndipo iwo akudziwa dzina lanu adzakhulupirira Inu; pakuti, Inu Yehova, simunawasiye iwo akufuna Inu.


Ndipo ataoloka iwo, anafika pamtunda ku Genesarete, nakocheza padooko.


nathamangira dziko lonselo nayamba kunyamula anthu odwala pa mphasa zao, kufika nao kumene anamva kuti analiko Iye.


Ndipo patachitika ichi, enanso a m'chisumbu, okhala nazo nthenda, anadza, nachiritsidwa;


kuti ndimzindikire Iye, ndi mphamvu ya kuuka kwake, ndi chiyanjano cha zowawa zake, pofanizidwa ndi imfa yake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa