Marko 5:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo Iye anaunguzaunguza kumuona iye amene adachita ichi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo Iye anaunguzaunguza kumuona iye amene adachita ichi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Koma Yesu adayang'anayang'ana kuti aone yemwe wachita zimenezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Koma Yesu anapitirizabe kuyangʼana kuti aone amene anachita zimenezi. Onani mutuwo |