Marko 4:4 - Buku Lopatulika4 ndipo kunali, m'kufesa kwake, zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndi mbalame zinadza ndi kuzitha kudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndipo kunali, m'kufesa kwake, zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndi mbalame zinadza ndi kuzitha kudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Akufesa choncho, mbeu zina zidagwera m'njira, ndipo mbalame zidabwera nkuzitolatola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Akufesa, mbewu zina zinagwera mʼmbali mwa njira, ndipo mbalame zinabwera ndi kuzidya. Onani mutuwo |