Marko 3:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Afarisi anatuluka, ndipo pomwepo anamkhalira upo ndi Aherode, wakumuononga Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Afarisi anatuluka, ndipo pomwepo anamkhalira upo ndi Aherode, wakumuononga Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamenepo Afarisi aja adatuluka nakachita upo ndi anthu a m'chipani cha Herode, kuti apangane njira yophera Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kenaka Afarisi anatuluka nayamba kukonza chiwembu ndi Aherode mmene angamuphere Yesu. Onani mutuwo |