Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 3:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo anthu ambiri anakhala pansi pomzinga; nanena kwa Iye, Onani, amanu ndi abale anu ali kunja akufunani Inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo anthu ambiri anakhala pansi pomzinga; nanena kwa Iye, Onani, amanu ndi abale anu ali kunja akufunani Inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Anthu ambirimbiri adaakhala pansi pomzungulira. Ndiye iwo aja adamuuza kuti, “Amai anu ndi abale anu ali panjapa, akukufunani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Gulu la anthu linakhala momuzungulira Iye, ndipo anamuwuza kuti, “Amayi ndi abale anu ali panja akukufunani.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 3:32
3 Mawu Ofanana  

Koma Iye anayankha, nati kwa iye wonenayo, Amai wanga ndani, ndipo abale anga ndi ayani?


Ndipo anadza amake ndi abale ake; naima kunja, namtumira uthenga kumuitana.


Ndipo anawayankha nanena, Amai wanga ndi abale anga ndani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa