Marko 3:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo anawayankha nanena, Amai wanga ndi abale anga ndani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo anawayankha nanena, Amai wanga ndi abale anga ndani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Koma Iye adati, “Amai anga! Abale anga! Otinso?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Iye anafunsa kuti, “Amayi ndi abale anga ndi ndani?” Onani mutuwo |