Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 3:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo anawayankha nanena, Amai wanga ndi abale anga ndani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo anawayankha nanena, Amai wanga ndi abale anga ndani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Koma Iye adati, “Amai anga! Abale anga! Otinso?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Iye anafunsa kuti, “Amayi ndi abale anga ndi ndani?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 3:33
9 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene abale ake anamva, anadza kudzamgwira Iye; pakuti anati adayaluka.


Ndipo anthu ambiri anakhala pansi pomzinga; nanena kwa Iye, Onani, amanu ndi abale anu ali kunja akufunani Inu.


Ndipo anawaunguzaunguza iwo akumzingawo, nanena, Taonani, amai wanga ndi abale anga.


Si mmisiri wa mitengo uyu, mwana wa Maria, mbale wao wa Yakobo, ndi Yose, ndi Yudasi, ndi Simoni? Ndipo alongo ake sali nafe pano kodi? Ndipo anakhumudwa ndi Iye.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Kuli bwanji kuti munalikundifunafuna Ine? Simunadziwa kodi kuti kundiyenera Ine ndikhale m'zake za Atate wanga?


Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.


Kotero kuti ife sitidziwanso munthu tsopano monga mwa thupi; ndipo ngati tazindikira Khristu monga mwa thupi, koma tsopano sitimzindikiranso motero.


amene anati za atate wake ndi amai wake, sindinamuone; Sanazindikire abale ake, sanadziwe ana ake omwe; popeza anasamalira mau anu, nasunga chipangano chanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa