Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 3:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo Satana akadziukira mwini yekha, nagawanika, sangathe kukhazikika, koma atsirizika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo Satana akadziukira mwini yekha, nagawanika, sakhoza kukhazikika, koma atsirizika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Tsono ngati a mu ufumu wa Satana aukirana okhaokha nagaŵikana, Satanayo sangalimbe, ndiye kuti watha basi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Ndipo ngati Satana adzitsutsa yekha sangathe kuyima; ulamuliro wake watha.

Onani mutuwo Koperani




Marko 3:26
2 Mawu Ofanana  

Pomwepo Yesu ananena kwa iye, Choka Satana, pakuti kwalembedwa, Ambuye Mulungu wako udzamgwadira, ndipo Iye yekhayekha udzamlambira.


Ndipo nyumba ikagawanika pa iyo yokha, singathe kukhazikika nyumbayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa