Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 2:11 - Buku Lopatulika

11 Ndikuuza iwe, Nyamuka, senza mphasa yako, numuke kwanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndikuuza iwe, Nyamuka, senza mphasa yako, numuke kwanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 “Iwe, dzuka, tenga machira ako, uzipita kumudzi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 “Ndikuwuza iwe, imirira, tenga mphasa yako ndipo pita kwanu.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 2:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anagwidwa chifundo, natansa dzanja namkhudza iye, nanena naye, Ndifuna; khala wokonzedwa.


Koma kuti mudziwe kuti Mwana wa Munthu ali mwini ulamuliro wakukhululukira machimo padziko lapansi (ananena ndi wodwala manjenje),


Ndipo ananyamuka iye pomwepo, nasenza mphasa, natuluka pamaso pa iwo onse; kotero kuti anadabwa onse, nalemekeza Mulungu, nanena kuti, Zotere sitinazione ndi kale lonse.


Wopatsa moyo ndi mzimu; thupi silithandiza konse. Mau amene ndalankhula ndi inu ndiwo mzimu, ndi moyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa