Marko 16:16 - Buku Lopatulika16 Amene akhulupirira nabatizidwa, adzapulumutsidwa; koma amene sakhulupirira adzalangidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Amene akhulupirira nabatizidwa, adzapulumutsidwa; koma amene sakhulupirira adzalangidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Amene akakhulupirire ndi kubatizidwa, adzapulumuka, koma amene sakakhulupirira, adzaweruzidwa kuti ngwolakwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Aliyense amene akakhulupirire nabatizidwa adzapulumuka, koma amene sakakhulupirira adzalangidwa. Onani mutuwo |