Marko 16:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ananena nao, Mukani kudziko lonse lapansi, lalikirani Uthenga Wabwino kwa olengedwa onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ananena nao, Mukani kudziko lonse lapansi, lalikirani Uthenga Wabwino kwa olengedwa onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono adaŵauza kuti, “Pitani ku dziko lonse lapansi, kalalikireni anthu onse Uthenga Wabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Anati kwa iwo, “Pitani mʼdziko lonse lapansi ndipo mukalalikire Uthenga Wabwino kwa zolengedwa zonse. Onani mutuwo |