Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:44 - Buku Lopatulika

44 Ndipo Pilato anazizwa ngati adamwaliradi; naitana kenturiyo, namfunsa ngati adamwalira kale.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Ndipo Pilato anazizwa ngati adamwaliradi; naitana kenturiyo, namfunsa ngati adamwalira kale.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Pilato adaadabwa kumva kuti Yesu wafa kale. Choncho adaitanitsa mkulu wa asilikali uja, namufunsa kuti, “Kodi Yesu wafa kaledi?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Pilato anadabwa pakumva kuti anali atamwalira kale. Anayitana Kenturiyo, namufunsa ngati Yesu anali atamwalira kale.

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:44
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pakumva ichi, Yesu anazizwa, nati kwa iwo akumtsata, Indetu ndinena kwa inu, ngakhale mwa Israele, sindinapeze chikhulupiriro chotere.


anadzapo Yosefe wa ku Arimatea, mkulu wa milandu womveka, amene yekha analikuyembekezera Ufumu wa Mulungu; nalimba mtima nalowa kwa Pilato, napempha mtembo wake wa Yesu.


Ndipo pamene anachidziwa ndi kenturiyo, anamninkha Yosefe mtembowo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa