Marko 15:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo pamene anachidziwa ndi kenturiyo, anamninkha Yosefe mtembowo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo pamene anachidziwa ndi kenturiyo, anamninkha Yosefe mtembowo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Mkulu wa asilikaliyo atavomera, Pilato adamlola Yosefe kuti akatenge mtembowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Atawuzidwa ndi Kenturiyo kuti zinali motero, anapereka mtembowo kwa Yosefe. Onani mutuwo |