Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 15:45 - Buku Lopatulika

45 Ndipo pamene anachidziwa ndi kenturiyo, anamninkha Yosefe mtembowo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 Ndipo pamene anachidziwa ndi kenturiyo, anamninkha Yosefe mtembowo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Mkulu wa asilikaliyo atavomera, Pilato adamlola Yosefe kuti akatenge mtembowo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Atawuzidwa ndi Kenturiyo kuti zinali motero, anapereka mtembowo kwa Yosefe.

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:45
5 Mawu Ofanana  

yemweyo anapita kwa Pilato, napempha mtembo wa Yesu. Pomwepo Pilato analamula kuti uperekedwe.


Ndipo pamene kenturiyo, woimirirapo popenyana ndi Iye, anaona kuti anapereka mzimu kotero, anati, Zoonadi, munthu uyu anali Mwana wa Mulungu.


Ndipo Pilato anazizwa ngati adamwaliradi; naitana kenturiyo, namfunsa ngati adamwalira kale.


Ndipo anagula bafuta, namtsitsa Iye, namkulunga m'bafutamo, namuika m'manda osemedwa m'thanthwe; nakunkhunizira mwala pakhomo la manda.


Chitatha ichi Yosefe wa ku Arimatea, ndiye wophunzira wa Yesu, koma mobisika, chifukwa cha kuopa Ayuda, anapempha Pilato kuti akachotse mtembo wa Yesu. Ndipo Pilato analola. Chifukwa chake anadza, nachotsa mtembo wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa