Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Pilato anamfunsanso, nanena, Suyankha kanthu kodi? Taona, akunenera Iwe zinthu zambiri zotere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Pilato anamfunsanso, nanena, Suyankha kanthu kodi? Taona, akunenera Iwe zinthu zambiri zotere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Pilato adamufunsanso kuti, “Kodi ulibe poyankha? Ona zonse zimene akukunenezazi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndipo Pilato anamufunsanso Iye kuti, “Kodi Iwe suyankhapo kanthu? Tamva zinthu zambiri akukunenerazi.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo mkulu wa ansembe anaimirira, nati kwa Iye, Suvomera kanthu kodi? Nchiyani ichi chimene awa akunenera Iwe?


Pomwepo Pilato ananena kwa Iye, Sukumva kodi zinthu zambiri zotere akunenera Iwe?


Ndipo ansembe aakulu anamnenera Iye zinthu zambiri.


Koma Yesu sanayankhenso kanthu; kotero kuti Pilato anazizwa.


Chifukwa chake Pilato ananena kwa Iye, Simulankhula ndi ine kodi? Simudziwa kodi kuti ulamuliro ndili nao wakukumasulani, ndipo ndili nao ulamuliro wakukupachikani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa