Marko 15:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Pilato anamfunsanso, nanena, Suyankha kanthu kodi? Taona, akunenera Iwe zinthu zambiri zotere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Pilato anamfunsanso, nanena, Suyankha kanthu kodi? Taona, akunenera Iwe zinthu zambiri zotere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pilato adamufunsanso kuti, “Kodi ulibe poyankha? Ona zonse zimene akukunenezazi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndipo Pilato anamufunsanso Iye kuti, “Kodi Iwe suyankhapo kanthu? Tamva zinthu zambiri akukunenerazi.” Onani mutuwo |