Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 14:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo ophunzira anatuluka, nafika m'mzinda, napeza monga anati kwa iwo; ndipo anakonza Paska.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo ophunzira anatuluka, nafika m'mzinda, napeza monga anati kwa iwo; ndipo anakonza Paska.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ophunzira aja adanyamuka naloŵa mumzindamo. Adachipezadi monga momwe Yesu adaaŵauzira, ndipo adakonza za phwando la Paska.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ophunzirawo anachoka, napita mu mzindawo ndipo anakapeza zinthu monga mmene Yesu anawawuzira. Choncho anakakonza Paska.

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:16
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinachita monga momwe anandilamulira, ndinatulutsa akatundu anga usana, ngati a pa ulendo wa kundende, ndi madzulo ndinaboola pakhoma ndi dzanja langa, ndinawatulutsa pali mdima, ndi kuwasenza paphewa panga pamaso pao.


Ndipo iye yekha adzakusonyezani chipinda chapamwamba chachikulu choyalamo ndi chokonzedwa; ndipo m'menemo mutikonzere.


Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.


Ndipo anapita iwo, napeza monga adatero nao; ndipo anakonza Paska.


Ndipo anati kwa iwo, Pamene ndinakutumizani opanda thumba la ndalama, ndi thumba la kamba, ndi nsapato, munasowa kanthu kodi? Anati iwo, Iai.


Koma zinthu izi ndalankhula ndi inu kuti ikadza nthawi yao, mukakumbukire kuti ndinakuuzani. Koma izi sindinanene kwa inu kuyambira pachiyambi, chifukwa ndinali pamodzi ndi inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa