Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 14:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo pofika madzulo anadza Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Kutada, Yesu adabwera ndi ophunzira ake khumi ndi aŵiri aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ndipo kutada Yesu anafika ndi khumi ndi awiriwo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 14:17
7 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzira anatuluka, nafika m'mzinda, napeza monga anati kwa iwo; ndipo anakonza Paska.


Ndipo pamene anaseama iwo kudya, Yesu anati, Ndithu ndinena ndi inu, Mmodzi wa inu adzandipereka Ine, ndiye wakudya ndi Ine pamodzi.


Ndipo itadza nthawi yake, Iye anakhala pachakudya, ndi ophunzira pamodzi ndi Iye.


Sindinena za inu nonse; ndidziwa amene ndawasankha: koma kuti cholemba chikwaniridwe, Iye wakudya mkate wanga anatsalimira pa Ine chidendene chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa