Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 11:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo Iye analowa mu Yerusalemu, mu Kachisi; ndipo m'mene anaunguza zinthu zonse, popeza ndi madzulo, anatuluka kupita ku Betaniya pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo Iye analowa m'Yerusalemu, m'Kachisi; ndipo m'mene anaunguza zinthu zonse, popeza ndi madzulo, anatuluka kupita ku Betaniya pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Yesu ataloŵa m'Yerusalemu, adakaloŵa m'Nyumba ya Mulungu, nayang'anayang'ana zonse. Tsono poti chisisira chinali chitagwa, adatuluka napita ku Betaniya pamodzi ndi ophunzira ake khumi ndi aŵiri aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Yesu analowa mu Yerusalemu napita ku Nyumba ya Mulungu. Anayangʼana zonse, koma popeza kuti nthawi inali itapita, anatuluka kupita ku Betaniya pamodzi ndi khumi ndi awiriwo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 11:11
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa ine, Lowa, kapenye zonyansa zoipa alikuzichita komweko.


Ndipo kudzachitika nthawi yomweyi kuti ndidzasanthula Yerusalemu ndi nyali, ndipo ndidzalanga amunawo okhala ndi nsenga, onena m'mtima mwao, Yehova sachita chokoma, kapena kuchita choipa.


Taonani, ndituma mthenga wanga, kuti akonzeretu njira pamaso panga; ndipo Ambuye amene mumfuna adzadza ku Kachisi wake modzidzimutsa; ndiye mthenga wa chipangano amene mukondwera naye; taonani akudza, ati Yehova wa makamu.


Ndipo masiku onse madzulo anatuluka Iye m'mzinda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa