Marko 10:44 - Buku Lopatulika44 ndipo aliyense amene afuna kukhala woyamba mwa inu adzakhala kapolo wa onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 ndipo amene aliyense afuna kukhala woyamba mwa inu adzakhala kapolo wa onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Ndipo aliyense wofuna kukhala mtsogoleri pakati panu, azikhala kapolo wa onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 ndipo aliyense amene akufuna kukhala wamkulu akhale kapolo wa onse. Onani mutuwo |