Marko 10:43 - Buku Lopatulika43 Koma mwa inu sikutero ai; koma aliyense amene afuna kukhala wamkulu mwa inu adzakhala mtumiki wanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Koma mwa inu sikutero ai; koma amene aliyense afuna kukhala wamkulu mwa inu adzakhala mtumiki wanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Koma pakati pa inu zisamatero ai. Aliyense wofuna kukhala mkulu pakati panu, azikhala mtumiki wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Sizili choncho ndi inu. Mʼmalo mwake, amene akufuna kukhala wamkulu pakati panu ayenera kukhala wotumikira, Onani mutuwo |