Marko 10:34 - Buku Lopatulika34 ndipo adzamnyoza Iye, nadzamthira malovu, nadzamkwapula Iye, nadzamupha; ndipo pofika masiku atatu adzauka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 ndipo adzamnyoza Iye, nadzamthira malovu, nadzamkwapula Iye, nadzamupha; ndipo pofika masiku atatu adzauka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Amenewo akamchita chipongwe, akamthira malovu, akamkwapula nkumupha. Koma patapita masiku atatu, Iye adzauka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 amene adzamuchita chipongwe ndi kumuthira malovu, kumukwapula ndi kumupha. Patatha masiku atatu adzauka.” Onani mutuwo |