Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo anadabwa, nanena kwa Iye, Ndipo angathe kupulumuka ndani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo anadabwa, nanena kwa Iye, Ndipo angathe kupulumuka ndani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Pamenepo ophunzira aja adazizwa koposa, nayamba kufunsana kuti, “Tsono nanga angathe kupulumuka ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Ophunzira anadabwa kwambiri, ndipo anati kwa wina ndi mnzake, “Nanga ndani amene angapulumuke?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:26
9 Mawu Ofanana  

Nkwa pafupi kuti ngamira ipyole diso la singano kuposa kuti mwini chuma alowe mu Ufumu wa Mulungu.


Yesu anawayang'ana iwo nati, Sikutheka ndi anthu, koma kutheka ndi Mulungu; pakuti zinthu zonse zitheka ndi Mulungu.


Ndipo Iye anakwera, nalowa kwa iwo m'ngalawa, ndipo mphepo inaleka; ndipo anadabwa kwakukulu mwa iwo okha;


Ndipo anadabwa kwakukulukulu, nanena, Wachita Iye zonse bwino; angakhale ogontha awamvetsa, ndi osalankhula awalankhulitsa.


Ndipo munthu anati kwa Iye, Ambuye, akupulumutsidwa ndiwo owerengeka kodi? Koma Iye anati kwa iwo,


Koma akumvawo anati, Tsono ndani angathe kupulumutsidwa?


Ndipo iwo anati, Ukhulupirire Ambuye Yesu, ndipo udzapulumuka, iwe ndi apabanja ako.


Kodi ali atumiki a Khristu? (Ndilankhula monga moyaluka), makamaka ine; m'zivutinso mochulukira, m'ndende mochulukira, m'mikwingwirima mosawerengeka, muimfa kawirikawiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa