Marko 10:25 - Buku Lopatulika25 Nkwa pafupi kuti ngamira ipyole diso la singano kuposa kuti mwini chuma alowe mu Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Nkwa pafupi kuti ngamira ipyole diso la singano kuposa kuti mwini chuma alowe mu Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Nkwapafupi kuti ngamira idzere pa kachiboo ka zingano, kupambana kuti munthu wachuma akaloŵe mu Ufumu wa Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ndi kwapafupi kwa ngamira kuti idzere pa kabowo ka zingano kusiyana ndi munthu wachuma kuti alowe mu ufumu wa Mulungu.” Onani mutuwo |