Marko 10:22 - Buku Lopatulika22 Koma nkhope yake inagwa pa mau awa, ndipo anachoka iye wachisoni; pakuti anali mwini chuma chambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma nkhope yake inagwa pa mau awa, ndipo anachoka iye wachisoni; pakuti anali mwini chuma chambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Atamva zimenezo, munthu uja nkhope yake idagwa, adangochokapo ali wovutika mu mtima, chifukwa adaali munthu wa chuma chambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Pa chifukwa ichi nkhope yake inagwa. Anachoka ali wachisoni, chifukwa anali ndi chuma chambiri. Onani mutuwo |