Marko 10:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Atatero adayamba kuŵafungata anawo, naŵasanjika manja ndi kuŵadalitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo ananyamula ana mʼmanja ake, ndi kuyika manja ake pa iwo nawadalitsa. Onani mutuwo |