Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Atatero adayamba kuŵafungata anawo, naŵasanjika manja ndi kuŵadalitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ndipo ananyamula ana mʼmanja ake, ndi kuyika manja ake pa iwo nawadalitsa.

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:16
8 Mawu Ofanana  

Iye adzadyetsa zoweta zake ngati mbusa, nadzasonkhanitsa anaankhosa m'manja mwake, nadzawatengera pa chifuwa chake, ndipo adzatsogolera bwinobwino zimene ziyamwitsa.


Ndipo pamene iwo analikudya, Iye anatenga mkate, ndipo pamene anadalitsa, ananyema, napereka kwa iwo, kuti, Tengani; thupi langa ndi ili.


Ndipo anatenga kamwana, nakaika pakati pao, nakayangata, nanena nao,


Mudzakhala odala m'mzinda, ndi odala kubwalo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa