Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:15 - Buku Lopatulika

15 Ndithu ndinena ndi inu, Munthu aliyense wosalandira Ufumu wa Mulungu ngati kamwana, sadzalowamo konse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndithu ndinena ndi inu, Munthu aliyense wosalandira Ufumu wa Mulungu ngati kamwana, sadzalowamo konse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Ndithu ndikunenetsa kuti yemwe salandira Ufumu wa Mulungu ngati mwana, ameneyo sadzaloŵamo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Ndikukuwuzani choonadi, aliyense amene sadzalandira Ufumu wa Mulungu ngati kamwana sadzalowamo.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:15
6 Mawu Ofanana  

nati, Indetu ndinena kwa inu, Ngati simutembenuka, nimukhala monga tianato, simudzalowa konse mu Ufumu wa Kumwamba.


Koma Yesu anati, Tilekeni tiana, musatikanize kudza kwa Ine: chifukwa Ufumu wa Kumwamba uli wa totere.


Indetu ndinena kwa inu, Aliyense wosalandira Ufumu wa Mulungu ngati mwana, sadzalowamo ndithu.


Abale, musakhale ana m'chidziwitso, koma m'choipa khalani makanda, koma m'chidziwitso akulu misinkhu.


lirani monga makanda alero mkaka woyenera, wopanda chinyengo, kuti mukakule nao kufikira chipulumutso;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa