Marko 10:15 - Buku Lopatulika15 Ndithu ndinena ndi inu, Munthu aliyense wosalandira Ufumu wa Mulungu ngati kamwana, sadzalowamo konse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndithu ndinena ndi inu, Munthu aliyense wosalandira Ufumu wa Mulungu ngati kamwana, sadzalowamo konse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndithu ndikunenetsa kuti yemwe salandira Ufumu wa Mulungu ngati mwana, ameneyo sadzaloŵamo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndikukuwuzani choonadi, aliyense amene sadzalandira Ufumu wa Mulungu ngati kamwana sadzalowamo.” Onani mutuwo |