Maliro 2:1 - Buku Lopatulika1 Ambuye waphimbatu ndi mtambo mwana wamkazi wa Ziyoni, pomkwiyira! Wagwetsa pansi kuchokera kumwamba kukoma kwake kwa Israele; osakumbukira poponda mapazi ake tsiku la mkwiyo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ambuye waphimbatu ndi mtambo mwana wamkazi wa Ziyoni, pomkwiyira! Wagwetsa pansi kuchokera kumwamba kukoma kwake kwa Israele; osakumbukira poponda mapazi ake tsiku la mkwiyo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta wakwiya kwambiri, taonani m'mene waphimbira Ziyoni ndi mdima! Ulemerero wa Israele wautaya pansi kuuchotsa Kumwamba. Pa tsiku la mkwiyo wake sadakumbukirenso kuti Ziyoni anali ngati mphondero yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Haa, Ambuye waphimba mwana wamkazi wa Ziyoni ndi mtambo wa mkwiyo wake! Iye wataya pansi ulemerero wa Israeli kuchoka kumwamba. Pa tsiku la mkwiyo wake Iye sanakumbukirenso popondapo mapazi ake. Onani mutuwo |