Maliro 1:3 - Buku Lopatulika3 Yuda watengedwa ndende chifukwa cha msauko ndi ukapolo waukulu; akhala mwa amitundu, sapeza popuma; onse akumlondola anampeza pakati popsinjikiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Yuda watengedwa ndende chifukwa cha msauko ndi ukapolo waukulu; akhala mwa amitundu, sapeza popuma; onse akumlondola anampeza pakati popsinjikiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ayuda apita ku ukapolo kukazunzika, ndi kukagwira ntchito yakalavulagaga. Akukhala m'maiko ena, osaona malo opumulira. Onse oŵapirikitsa aŵapeza, ali pa mavuto zedi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yuda watengedwa ku ukapolo, kukazunzika ndi kukagwira ntchito yolemetsa. Iye akukhala pakati pa anthu a mitundu ina; ndipo alibe malo opumulira. Onse omuthamangitsa iye amupitirira, ndipo alibe kwina kothawira. Onani mutuwo |