Maliro 1:4 - Buku Lopatulika4 M'njira za Ziyoni mulira posoweka akudzera msonkhano; pa zipata zake zonse papasuka; ansembe ake onse ausa moyo; anamwali ake asautsidwa; iye mwini namva zowawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 M'njira za Ziyoni mulira posoweka akudzera msonkhano; pa zipata zake zonse papasuka; ansembe ake onse ausa moyo; anamwali ake asautsidwa; iye mwini namva zowawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Miseu yopita ku Ziyoni yaŵirira, chifukwa palibe wopitako kuti akapembedze pa masiku achikondwerero. Zipata zake zonse zili pululu, ansembe ake akungodandaula. Anamwali ake aja mtima wao ukupweteka, ndithu Ziyoni ali pa masautso oopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Misewu yopita ku Ziyoni ikulira, chifukwa palibe ndi mmodzi yemwe akubwera ku maphwando ake. Zipata zake zonse zili pululu, ansembe akubuwula. Anamwali ake akulira, ndipo ali mʼmasautso woopsa. Onani mutuwo |