Malaki 3:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti Ine Yehova sindisinthika, chifukwa chake inu ana a Yakobo simunathedwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti Ine Yehova sindisinthika, chifukwa chake inu ana a Yakobo simunathedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Ine ndine Chauta, wosasinthika. Nchifukwa chake inu zidzukulu za Yakobe simudaonongeke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Ine ndine Yehova, ndipo sindisintha. Choncho inu zidzukulu za Yakobo, simunawonongedwe. Onani mutuwo |