Malaki 3:4 - Buku Lopatulika4 Pamenepo chopereka cha Yuda ndi Yerusalemu chidzakomera Yehova, ngati masiku a kale lija, ndi ngati zaka zoyamba zija. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pamenepo chopereka cha Yuda ndi Yerusalemu chidzakomera Yehova, ngati masiku a kale lija, ndi ngati zaka zoyamba zija. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Choncho nsembe za Yuda ndi za Yerusalemu zidzakondweretsa Chauta, monga zidaaliri masiku amakedzana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 ndipo Yehova adzalandira zopereka za Yuda ndi Yerusalemu, ngati masiku akale, masiku amakedzana. Onani mutuwo |