Malaki 1:3 - Buku Lopatulika3 koma Esau ndinamuda, ndinasanduliza mapiri ake abwinja, ndi kupereka cholowa chake kwa ankhandwe a m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 koma Esau ndinamuda, ndinasanduliza mapiri ake abwinja, ndi kupereka cholowa chake kwa ankhandwe a m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Komabe ndakonda Yakobe, koma Esau ndadana naye. Dziko lake lamapiri ndalisandutsa chipululu, dziko limene ndidampatsa ndalisandutsa la nkhandwe zam'chipululu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 koma ndinamuda Esau, ndipo dziko lake lamapiri ndalisandutsa chipululu ndipo cholowa chake ndasiyira ankhandwe a mʼchipululu.” Onani mutuwo |