Machitidwe a Atumwi 8:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo makamuwo ndi mtima umodzi anasamalira zonenedwa ndi Filipo, pamene anamva, napenya zizindikiro zimene anazichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo makamuwo ndi mtima umodzi anasamalira zonenedwa ndi Filipo, pamene anamva, napenya zizindikiro zimene anazichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Makamu a anthu ndi mtima umodzi ankatchera makutu ku zimene Filipo ankanena. Onse ankamvetsera mau ake nkumaona zozizwitsa zimene iye ankachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Gulu la anthu litamva Filipo akulalikira komanso kuona zizindikiro zozizwitsa zimene ankazichita, onse anamvetsetsa zimene iye amanena. Onani mutuwo |