Machitidwe a Atumwi 8:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Filipo anatsikira kumzinda wa ku Samariya, nawalalikira iwo Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Filipo anatsikira kumudzi wa ku Samariya, nawalalikira iwo Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Filipo adatsikira ku mzinda wa ku Samariya, namalalikira anthu akumeneko za Khristu, Mpulumutsi wolonjezedwa uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Filipo anapita ku mzinda wa ku Samariya ndipo analalikira za Khristu kumeneko. Onani mutuwo |