Machitidwe a Atumwi 7:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo makolo aakuluwa podukidwa naye Yosefe, anamgulitsa amuke naye ku Ejipito; ndipo Mulungu anali naye, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo makolo akuluwa podukidwa naye Yosefe, anamgulitsa amuke naye ku Ejipito; ndipo Mulungu anali naye, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Tsono makolo athuwo adachita nsanje ndi mbale wao Yosefe, ndipo adamgulitsa kuti akakhale kapolo ku Ejipito. Koma Mulungu anali naye, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Makolo athu anachita nsanje ndi Yosefe ndipo anamugulitsa kuti akakhale kapolo ku Igupto. Koma Mulungu anali naye Onani mutuwo |