Machitidwe a Atumwi 7:52 - Buku Lopatulika52 Ndiye yani wa aneneri makolo anu sanamzunze? Ndipo anawapha iwo amene anaonetseratu za kudza kwake kwa Wolungamayo; wa Iye amene mwakhala tsopano akumpereka ndi akumupha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Ndiye yani wa aneneri makolo anu sanamzunza? Ndipo anawapha iwo amene anaonetseratu za kudza kwake kwa Wolungamayo; wa Iye amene mwakhala tsopano akumpereka ndi akumupha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Kodi alipo mneneri ndi mmodzi yemwe amene makolo anu aja sadamzunze? Iyai, iwo adapha anthu amene ankaneneratu za kudza kwake kwa Wolungama uja. Tsopano inuyo mudampereka kwa adani ake ndi kumupha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Kodi analipo mneneri amene makolo anu sanamuzunze? Iwo anapha ngakhale amene ananeneratu za kubwera kwa Wolungamayo. Ndipo tsopano inu munamupereka ndi kumupha Iye. Onani mutuwo |