Machitidwe a Atumwi 7:32 - Buku Lopatulika32 akuti, Ine ndine Mulungu wa makolo anu, Mulungu wa Abrahamu, ndi wa Isaki, ndi wa Yakobo. Ndipo Mose ananthunthumira, osalimbika mtima kupenyetsako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 akuti, Ine ndine Mulungu wa makolo anu, Mulungu wa Abrahamu, ndi wa Isaki, ndi wa Yakobo. Ndipo Mose ananthunthumira, osalimbika mtima kupenyetsako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 ‘Ine ndine Mulungu wa makolo ako, Mulungu wa Abrahamu, Isaki, ndi Yakobe.’ Mose adayamba kunjenjemera mwakuti sadalimbenso mtima kuti nkupenyako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 ‘Ine ndine Mulungu wa makolo ako, Mulungu wa Abrahamu, Isake ndi Yakobo.’ Mose ananjenjemera chifukwa cha mantha ndipo sanalimbe mtima kuyangʼananso. Onani mutuwo |