Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:12 - Buku Lopatulika

12 Koma pakumva Yakobo kuti muli tirigu mu Ejipito, anatuma makolo athu ulendo woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Koma pakumva Yakobo kuti muli tirigu m'Ejipito, anatuma makolo athu ulendo woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Pamene Yakobe adamva kuti ku Ejipito kuli tirigu, adatumako makolo athu aja. Uwu unali ulendo wao woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Pamene Yakobo anamva kuti ku Igupto kunali tirigu, iye anatuma makolo athu ulendo woyamba.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:12
2 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene atatha kudya tirigu yense anatengayo ku Ejipito atate wao anati kwa iwo, Pitaninso, mukatigulire ife chakudya pang'ono.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa